2 Mafumu 9:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Yehu anatulukira kwa anyamata a mbuye wake, nanena naye wina, Mtendere kodi? Anakudzera chifukwa ninji wamisala uyu? Nanena nao, Mumdziwa munthuyo ndi makambidwe ake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Yehu anatulukira kwa anyamata a mbuye wake, nanena naye wina, Mtendere kodi? Anakudzera chifukwa ninji wamisala uyu? Nanena nao, Mumdziwa munthuyo ndi makambidwe ake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono Yehu atatuluka kubwerera kwa atsogoleri anzake aja, iwo adamufunsa kuti, “Kodi nkwabwino? Wamsala uja anadzatani kwa inu?” Yehu adayankha kuti “Ai, mukumdziŵa munthu wotere ndi zolankhula zake zomwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehu atatuluka kupita kumene kunali atsogoleri anzake, mmodzi mwa iwo anamufunsa kuti, “Kodi zonse zili bwino? Kodi munthu wamisala uja anabwera kudzatani kwa iwe?” Yehu anayankha kuti, “Iwe ukumudziwa munthu uja ndiponso ukudziwa zomwe amayankhula.” Onani mutuwo |