Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 9:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo agalu adzamudya Yezebele pa dera la Yezireele, wopanda wina wakumuika. Pamenepo anatsegula pakhomo, nathawa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo agalu adzamudya Yezebele pa dera la Yezireele, wopanda wina wakumuika. Pamenepo anatsegula pakhomo, nathawa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Ndipo agalu adzamudya Yezebele ku dziko la Yezireele. Palibe ndi mmodzi yemwe amene adzamuike.” Atanena mau amenewo, mneneri uja adatsekula chitseko, nathaŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Kunena za Yezebeli, agalu adzamudya ku dera la Yezireeli ndipo palibe amene adzamuyike mʼmanda.’ ” Kenaka mneneriyo anatsekula chitseko nʼkuthawa.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 9:10
6 Mawu Ofanana  

Ndipo za Yezebele yemwe Yehova ananena, nati, Agalu adzadya Yezebele ku linga la Yezireele.


Nutenge nsupa ya mafutayo, nuwatsanulire pamutu pake, nunene, Atero Yehova, Ndakudzoza iwe ukhale mfumu pa Israele. Utatero, tsegula pakhomo, nuthawe osachedwa,


Adzamuika monga kuika bulu, adzamkoka nadzamponya kunja kwa zipata za Yerusalemu.


ndi Yezireele, ndi Yokodeamu, ndi Zanowa;


Ndipo Ehudi anapulumuka pakuchedwa iwo, napitirira pa mafano osema, napulumuka kufikira Seira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa