Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 8:23 - Buku Lopatulika

23 Ndi machitidwe ena a Yoramu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndi machitidwe ena a Yoramu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwa kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono ntchito zina za Yehoramu, ndi zonse zimene adazichita, zidalembedwa m'buku la Mbiri ya Mafumu a ku Yuda.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Ndipo ntchito zina za Yehoramu ndi zonse zomwe anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Yuda?

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 8:23
16 Mawu Ofanana  

Ndipo machitidwe otsiriza a Solomoni, ndi ntchito zake zonse anazichita, ndi nzeru zake, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a Solomoni?


Tsono, machitidwe ake ena a Rehobowamu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Ndipo machitidwe onse ena a Asa, ndi mphamvu yake yonse, ndi zonse anazichita, ndi mizinda anaimanga, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda? Koma masiku a ukalamba wake anadwala mapazi ake.


Ndipo anyamata ake ananyamuka, napangana, nakantha Yowasi kunyumba ya Milo potsikira ku Sila.


Machitidwe ena tsono a Amaziya, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Yotamu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Azariya, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono adawachita Ahazi, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Hezekiya, ndi mphamvu yake yonse, ndi umo anamangira dziwe ndi mchera, nautengera mzinda madzi, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Manase, ndi zochimwa zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Amoni adawachita, sanalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Yosiya, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Machitidwe ena tsono a Yehoyakimu, ndi zonse anazichita, sizinalembedwe kodi m'buku la machitidwe a mafumu a Yuda?


Motero Aedomu anapanduka ku ulamuliro wa Yuda mpaka lero lino. Ndipo Alibina anapanduka nthawi yomweyi.


Nagona Yoramu ndi makolo ake, naikidwa pamodzi ndi makolo ake m'mzinda wa Davide; ndipo Ahaziya mwana wake anakhala mfumu m'malo mwake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa