2 Mafumu 8:22 - Buku Lopatulika22 Motero Aedomu anapanduka ku ulamuliro wa Yuda mpaka lero lino. Ndipo Alibina anapanduka nthawi yomweyi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Motero Aedomu anapanduka ku ulamuliro wa Yuda mpaka lero lino. Ndipo Alibina anapanduka nthawi yomweyi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Motero Aedomu ngoukira ulamuliro wa Yuda mpaka lero lino. Pa nthaŵi imeneyo mzinda wa Libina nawonso udaukira ulamuliro wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mpaka lero lino Edomu ndi wowukira Yuda. Nthawi yomweyo mzinda wa Libina unawukiranso. Onani mutuwo |