Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 8:14 - Buku Lopatulika

14 Ndipo anachoka kwa Elisa, nadza kwa mbuye wake; ameneyo ananena naye, Anakuuza chiyani Elisa? Nati iye, Anandiuza kuti mudzachira ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Ndipo anachoka kwa Elisa, nadza kwa mbuye wake; ameneyo ananena naye, Anakuuza chiyani Elisa? Nati iye, Anandiuza kuti mudzachira ndithu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Pomwepo Hazaeleyo adasiyana naye Elisa, napita kwa mbuyake. Mbuyakeyo adamufunsa kuti, “Kodi Elisa wakuuza zotani?” Hazaele adayankha kuti, “Inuyo muchira ndithu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Choncho Hazaeli anasiyana ndi Elisa ndi kubwerera kwa mbuye wake. Beni-Hadadi atafunsa kuti, “Elisa wakuwuza chiyani?” Hazaeli anayankha kuti, “Elisa wandiwuza kuti inu mudzachira ndithu.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 8:14
4 Mawu Ofanana  

Pamenepo analowa, naima kwa mbuye wake. Ndipo Elisa ananena naye, Ufuma kuti Gehazi? Nati, Ngati mnyamata wanu wayenda konse?


Nanena naye Elisa, Kamuuze, kuti, Sudzachira konse; popeza Yehova wandionetsa kuti adzafa ndithu.


Ndipo kunali m'mawa mwake, anatenga chimbwi, nachiviika m'madzi, nachiphimba pankhope pa mfumu, nifa; ndipo Hazaele analowa ufumu m'malo mwake.


Ndipo kuyambira pamenepo iye anafunafuna nthawi yabwino yakuti ampereke Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa