2 Mafumu 8:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anamyang'ana chidwi, mpaka anachita manyazi, nalira misozi munthu wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anamyang'ana chidwi, mpaka anachita manyazi, nalira misozi munthu wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Atatero, Elisa adamuyang'ana kwambiri Hazaele mpaka adachita manyazi. Apo Elisayo adayamba kulira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Elisa anamuyangʼana kwambiri Hazaeli mpaka anachita manyazi. Pamenepo munthu wa Mulungu anayamba kulira. Onani mutuwo |