2 Mafumu 8:10 - Buku Lopatulika10 Nanena naye Elisa, Kamuuze, kuti, Sudzachira konse; popeza Yehova wandionetsa kuti adzafa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Nanena naye Elisa, Kamuuze, kuti, Sudzachira konse; popeza Yehova wandionetsa kuti adzafa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Elisa adayankha kuti, “Chauta wandiwonetsa kuti adzafa, komabe pita ukamuuze kuti adzachira.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Elisa anayankha kuti, “Pita ndipo ukamuwuze kuti, ‘Udzachira ndithu,’ koma Yehova wandionetsa kuti adzafabe.” Onani mutuwo |