2 Mafumu 7:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo iye anaitana alonda ena, ndi iwo anafotokozera a m'nyumba ya mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo iye anaitana alonda ena, ndi iwo anafotokozera a m'nyumba ya mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Tsono alonda apachipata aja adalengeza uthengawo ndipo okhala kunyumba kwa mfumu adaumva. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Alonda a pa chipata aja analengeza uthengawu kwa okhala mʼnyumba yaufumu. Onani mutuwo |