Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 6:7 - Buku Lopatulika

7 Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Ndipo Elisa adati, “Kaitole.” Munthu uja adatambalitsa dzanja, naigwira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Elisa anati, “Itenge.” Ndipo munthuyo anatambalitsa dzanja lake nayitenga.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 6:7
7 Mawu Ofanana  

Pamenepo anaitana Gehazi, nati, Kaitane Msunamu uja. Namuitana. Ndipo atalowa kuli iye, anati, Nyamula mwana wako.


Pamenepo anadza, namfotokozera munthu wa Mulungu. Nati iye, Kagulitse mafuta, ukabwezere mangawa ako, ndi zotsalapo zikusunge iwe ndi ana ako.


Nati munthu wa Mulungu, Yagwera pati? Namuonetsapo yagwera. Pamenepo anadula kamtengo, nakaponya pomwepo, nayandamitsa nkhwangwayo.


Ndipo mfumu ya Aramu inalinkuchita nkhondo ndi Israele, nipangana ndi anyamata ake, kuti, Misasa yanga idzakhala pakutipakuti.


Koma Yehova anati kwa Mose, Tambasula dzanja lako, nuigwire kumchira; ndipo anatambasula dzanja lake, naigwira, nikhalanso ndodo m'dzanja lake;


Ndipo wakufayo anakhala tsonga, nayamba kulankhula. Ndipo anampereka kwa amake.


Ndipo Petro anamgwira dzanja, namnyamutsa; ndipo m'mene adaitana oyera mtima ndi amasiye, anampereka iye wamoyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa