Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 6:6 - Buku Lopatulika

6 Nati munthu wa Mulungu, Yagwera pati? Namuonetsapo yagwera. Pamenepo anadula kamtengo, nakaponya pomwepo, nayandamitsa nkhwangwayo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Nati munthu wa Mulungu, Yagwera pati? Namuonetsapo yagwera. Pamenepo anadula kamtengo, nakaponya pomwepo, nayandamitsa nkhwangwayo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Tsono munthu wa Mulungu uja adafunsa kuti, “Kodi yagwera pati?” Atamuwonetsa malowo, Elisa adadula kamtengo nakaponya pamadzipo, nkhwangwayo nkuyandama.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Ndipo munthu wa Mulungu uja anafunsa, “Yagwera pati?” Pamene anamuonetsa malowo, Elisa anadula kamtengo nakaponya pamenepo, ndipo nkhwangwayo inayandama.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 6:6
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anatuluka kunka ku magwero a madzi, nathiramo mchere, nati, Atero Yehova, Ndachiritsa madzi awa, sikudzafumirakonso imfa, kapena kusabalitsa.


Pamenepo anati, Bwera naoni ufa. Nathira m'nkhalimo; nati, Gawirani anthu kuti adye. Ndipo m'nkhalimo munalibe chowawa.


Ndipo wina analinkudula mtengo nkhwangwa inagwa m'madzi; ndipo anafuula, nati, Kalanga ine mbuyanga! Popeza njobwereka.


Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.


Ndipo iye anafuulira kwa Yehova; ndipo Yehova anamsonyeza mtengo ndipo anauponya m'madzimo, ndi madzi anasanduka okoma. Pamenepo anawapangira lemba ndi chiweruzo, ndi pomwepa anawayesa;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa