2 Mafumu 6:16 - Buku Lopatulika16 Nati iye, Usaopa, pakuti okhala pamodzi ndi ife achuluka koposa aja okhala pamodzi ndi iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Nati iye, Usaopa, pakuti okhala pamodzi ndi ife achuluka koposa aja okhala pamodzi ndi iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Elisa adati, “Usachite mantha, pakuti amene ali pa mbali yathu ngambiri kupambana m'mene aliri iwoŵa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mneneri anamuyankha kuti, “Usachite mantha. Amene ali mbali yathu ndi ambiri kupambana amene ali mbali yawo.” Onani mutuwo |