2 Mafumu 6:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ana a aneneri anati kwa Elisa, Taonani tsono, pamalo tikhalapo ife pamaso panu patichepera Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ana a aneneri anati kwa Elisa, Taonani tsono, pamalo tikhalapo ife pamaso panu patichepera Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Tsiku lina ena a m'gulu la aneneri adauza Elisa kuti, “Onani, malo tikukhala ndi inu ano akutichepera kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ana a aneneri anati kwa Elisa, “Taonani malo amene timakhala ndi inu atichepera kwambiri. Onani mutuwo |