2 Mafumu 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo anafika kwa mfumu ya Israele ndi kalata, yakuti, Pakulandira kalata iyi, taonani, ndatumiza Naamani mnyamata wanga kwa inu, kuti mumchiritse khate lake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo anafika kwa mfumu ya Israele ndi kalata, wakuti, Pakulandira kalata uyu, taonani, ndatumiza Naamani mnyamata wanga kwa inu, kuti mumchiritse khate lake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Atafika kwa mfumu ya ku Israele, adapereka kalata ija imene mau ake anali akuti, “Landirani kalatayi. Tsono amene ndakutumiziraniyo ndi Naamani mtumiki wanga, ndipo ndikufuna kuti inuyo mumchize khate lake.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kalata imene anapita nayo kwa mfumu ya ku Israeli inali ndi mawu awa: “Taonani, ndikutumiza Naamani mtumiki wanga pamodzi ndi kalatayi kwa inu kuti mumuchiritse khate lake.” Onani mutuwo |