2 Mafumu 5:16 - Buku Lopatulika16 Koma anati, Pali Yehova, amene ndiima pamaso pake, sindidzalandira kanthu. Ndipo anamkakamiza achilandire, koma anakana. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma anati, Pali Yehova, amene ndiima pamaso pake, sindidzalandira kanthu. Ndipo anamkakamiza achilandire, koma anakana. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Elisa adati, “Pali Chauta, Mulungu wamoyo, amene ndimamtumikira, ine sindilandira zimenezi.” Naamani adamkakamiza kuti atenge, koma iye adakana ndithu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Mneneri anayankha kuti, “Pali Yehova wamoyo, amene ine ndimamutumikira, sindidzalandira zimenezi.” Ndipo ngakhale Naamani anamukakamiza, iye anakanabe. Onani mutuwo |