2 Mafumu 5:13 - Buku Lopatulika13 Pamenepo anyamata ake anasendera, nanena naye, nati, Atate wanga, mneneri akadakuuzani chinthu chachikulu, simukadachichita kodi? Koposa kotani nanga ponena iye, Samba, nukonzeke? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pamenepo anyamata ake anasendera, nanena naye, nati, Atate wanga, mneneri akadakuuzani chinthu chachikulu, simukadachichita kodi? Koposa kotani nanga ponena iye, Samba, nukonzeke? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma atumiki ake adasendera pafupi namufunsa kuti, “Pepani bambo, kodi mneneri akadakulamulani chinthu chachikulu, inu simukadachita? Monga nchapatali kukasamba monga momwe mneneriyo wakuuziranimo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Antchito ake anamuyandikira namufunsa kuti, “Abambo anga, mneneri akanakulamulani chinthu chachikulu, kodi inu simukanachita? Nanga nʼzovuta motani zomwe mneneri wanena kuti ‘Kasambeni ndipo mudzayeretsedwa!’ ” Onani mutuwo |