2 Mafumu 5:12 - Buku Lopatulika12 Nanga Abana ndi Faripara, mitsinje ya Damasiko, siiposa kodi madzi onse a mu Israele? Ndilekerenji kukasamba m'mwemo, ndi kukonzeka? Natembenuka, nachoka molunda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Nanga Abana ndi Faripara, mitsinje ya Damasiko, siiposa kodi madzi onse a m'Israele? Ndilekerenji kukasamba m'mwemo, ndi kukonzeka? Natembenuka, nachoka molunda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kodi Abana ndi Faripara, mitsinje ya ku Damasiko, siposa mitsinje yonse ya ku Israele kuno? Monga sindikadatha kukasamba m'mitsinje imeneyo ndi kuchiritsidwa?” Pomwepo adapotoloka, nachokapo molunda. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kodi Abana ndi Faripara, mitsinje ya ku Damasiko, siyoposa mitsinje ina yonse ya ku Israeli? Kodi sindikanasamba mʼmitsinje imeneyo ndi kuyeretsedwa?” Kotero anatembenuka nachoka ali wokwiya kwambiri. Onani mutuwo |