2 Mafumu 5:11 - Buku Lopatulika11 Koma Naamani adapsa mtima, nachoka, nati, Taona, ndinati m'mtima mwanga, kutuluka adzanditulukira, nadzaima ndi kuitana pa dzina la Yehova Mulungu wake, ndi kuweyula dzanja lake pamalopo, ndi kuchiritsa wakhateyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Koma Naamani adapsa mtima, nachoka, nati, Taona, ndinati m'mtima mwanga, kutuluka adzanditulukira, nadzaima ndi kuitana pa dzina la Yehova Mulungu wake, ndi kuweyula dzanja lake pamalopo, ndi kuchiritsa wakhateyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Koma Naamani atamva zimenezi, adakwiya kwambiri nachokapo. Popita iye ankati, “Ha! Ine ndimaganiza kuti atuluka kubwera pano, ndipo aimirira natama dzina la Chauta Mulungu wake mopemba, naweyula dzanja lake pamwamba pa nthendapo, ndi kundichiritsa motero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Koma Naamani anachoka mokwiya ndipo anati, “Ine ndimaganiza kuti munthuyu atuluka ndipo ayimirira nayitana dzina la Yehova Mulungu wake, nayendetsa dzanja lake pamwamba pa nthendayi ndi kundichiritsa khate langa. Onani mutuwo |