2 Mafumu 5:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Elisa anamtumira mthenga, ndi kuti, Kasambe mu Yordani kasanu ndi kawiri, ndi mnofu wako udzabwerera momwe, nudzakhala wokonzeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Elisa anamtumira mthenga, ndi kuti, Kasambe m'Yordani kasanu ndi kawiri, ndi mnofu wako udzabwerera momwe, nudzakhala wokonzeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono Elisa adamtumira wamthenga kukamuuza kuti, “Pitani mukasambe mu mtsinje wa Yordani kasanunkaŵiri, ndipo muchira ndi kuyeretsedwa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Elisa anatumiza uthenga kwa iye woti, “Pita, kasambe kasanu ndi kawiri mu mtsinje wa Yorodani, thupi lako lidzachira ndi kukhalanso monga kale ndipo udzayeretsedwa.” Onani mutuwo |