Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 4:7 - Buku Lopatulika

7 Pamenepo anadza, namfotokozera munthu wa Mulungu. Nati iye, Kagulitse mafuta, ukabwezere mangawa ako, ndi zotsalapo zikusunge iwe ndi ana ako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pamenepo anadza, namfotokozera munthu wa Mulungu. Nati iye, Kagulitse mafuta, ukabwezere mangawa ako, ndi zotsalapo zikusunge iwe ndi ana ako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Tsono mai uja adapita kukafotokozera Elisa, munthu wa Mulungu uja. Ndipo Elisayo adauza maiyo kuti, “Mai, pitani mukagulitse mafutawo, ndipo mukabweze ngongole zanuzo. Tsono ndalama zotsala zikhale zothandizira inu ndi ana anu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Mayiyo anapita nakamuwuza munthu wa Mulungu amene anamuyankha kuti, “Pita, kagulitse mafutawo ndipo ukabweze ngongole ija. Ndalama zotsalazo zikakhale zako ndi ana ako.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 4:7
11 Mawu Ofanana  

Ndipo mau a Mulungu anafika kwa Semaya mneneri wa Mulungu, nati,


Ndipo anakwera, namgoneka pa kama wa munthu wa Mulungu, natuluka, namtsekera.


Ndipo mkaziyo anati kwa mwamuna wake, Taona, tsopano ndidziwa kuti munthu uyu wakupitira pathu pano chipitire ndiye munthu woyera wa Mulungu.


Nati, Katole. Natambasula dzanja lake, naitenga.


Ndipo munthu wa Mulunguyo anatuma mau kwa mfumu ya Israele, ndi kuti, Muchenjere musapite pakuti, popeza Aaramu alikutsikira uko.


Woipa akongola, wosabweza, koma wolungama achitira chifundo, napereka.


Musabwezere munthu aliyense choipa chosinthana ndi choipa. Ganiziranitu zinthu za ulemu pamaso pa anthu onse.


Chotsalira, abale, zinthu zilizonse zoona, zilizonse zolemekezeka, zilizonse zolungama, zilizonse zoyera, zilizonse zokongola, zilizonse zimveka zokoma; ngati kuli chokoma mtima china, kapena chitamando china, zilingirireni izi.


kuti mukayende oona mtima pa iwo a kunja, ndi kukhala osasowa kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa