2 Mafumu 4:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo pamene Elisa analowa m'nyumba, taonani, mwanayo ngwakufa, adamgoneka pakama pake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo pamene Elisa analowa m'nyumba, taonani, mwanayo ngwakufa, adamgoneka pakama pake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Elisa ataloŵa m'chipinda muja adaona mwana wakufayo atamgoneka pabedi pake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Ndipo Elisa atafika ku nyumbako, taonani, mwanayo anali wakufa atamugoneka pa bedi lake. Onani mutuwo |