2 Mafumu 4:30 - Buku Lopatulika30 Koma make wa mwana anati, Pali Yehova, pali inunso, ngati nkukusiyani. Ndipo ananyamuka, namtsata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma make wa mwana anati, Pali Yehova, pali inunso, ngati nkukusiyani. Ndipo ananyamuka, namtsata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Apo mai wake wa mwana uja adati, “Pali Chauta wamoyo, ndiponso pali inu nomwe, ine ndiye sindikusiyani ai.” Tsono Elisa adanyamuka natsatira maiyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Koma mayi wake wa mwana uja anati, “Pali Yehova wamoyo ndiponso pali inu nomwe, ineyo sindidzakusiyani.” Choncho Elisa ananyamuka natsatira mayiyo. Onani mutuwo |