2 Mafumu 4:26 - Buku Lopatulika26 uthamange tsopano kukomana naye, nunene naye, Muli bwino kodi? Mwamuna wanu ali bwino? Mwanayo ali bwino? Ndipo anati, Ali bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 uthamange tsopano kukomana naye, nunene naye, Muli bwino kodi? Mwamuna wanu ali bwino? Mwanayo ali bwino? Ndipo anati, Ali bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Thamanga msanga ukamchingamire, ndipo ukamufunse kuti, ‘Kodi nkwabwino? Kodi mwamuna wanu ali bwino? Nanga mwana uja ali bwino?’ ” Mkaziyo adayankha Gehazi kuti, “Inde, nkwabwino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Thamanga msanga ukakumane naye ndipo ukamufunse kuti, ‘Kodi muli bwino? Kodi mwamuna wanu ali bwino? Kodi mwana wanu ali bwino?’ ” Mayiyo anayankha kuti, “Zonse zili bwino.” Onani mutuwo |