2 Mafumu 4:25 - Buku Lopatulika25 Potero anamuka, nafika kwa munthu wa Mulungu kuphiri la Karimele. Ndipo kunali, pakumuona munthu wa Mulungu alinkudza kutali, anati kwa Gehazi mnyamata wake, Tapenya, suyo Msunamu uja; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Potero anamuka, nafika kwa munthu wa Mulungu kuphiri la Karimele. Ndipo kunali, pakumuona munthu wa Mulungu alinkudza kutali, anati kwa Gehazi mnyamata wake, Tapenya, suyo Msunamu uja; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Motero adayenda nakafika kwa Elisa, munthu wa Mulungu uja, ku phiri la Karimele. Tsono mneneri Elisa ataona kuti mai uja akudza, adauza Gehazi mtumiki wake kuti, “Taona patsidyapo, Msunamu uja akubwera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Choncho ananyamuka nakafika kwa munthu wa Mulungu uja ku Phiri la Karimeli. Munthu wa Mulungu ataona mayiyo patali, anawuza mtumiki wake Gehazi kuti, “Taona! Msunemu uyo! Onani mutuwo |