2 Mafumu 4:24 - Buku Lopatulika24 Pamenepo anamangirira bulu mbereko, nati kwa mnyamata wake, Kusa, tiye; usandilezetsa kuyendaku, ndikapanda kukuuza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Pamenepo anamangirira bulu mbereko, nati kwa mnyamata wake, Kusa, tiye; usandilezetsa kuyendaku, ndikapanda kukuuza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Pompo maiyo adaika chishalo nakwera bulu, ndipo adauza wantchitoyo kuti, “Thamangitsa buluyo. Usaleze mpaka ntakuuza.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Mayiyo anamangirira chishalo pa bulu ndipo anawuza wantchito wake kuti, “Yendetsa bulu mofulumira. Usachepetse liwiro pokhapokha nditakuwuza.” Onani mutuwo |