2 Mafumu 4:23 - Buku Lopatulika23 Ndipo anati, Ulikumuka kwa iye lero chifukwa ninji? Ngati mwezi wakhala, kapena mpa Sabata? Koma anati, Kuli bwino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Ndipo anati, Ulikumuka kwa iye lero chifukwa ninji? Ngati mwezi wakhala, kapena mpa Sabata? Koma anati, Kuli bwino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Apo mwamuna wakeyo adafunsa kuti, “Chifukwa chiyani mukupita kwa iyeyo lero? Lerotu si tsiku lokhala mwezi, kapenanso tsiku la Sabata ai.” Mai uja adati, “Palibe kanthu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Mwamuna wakeyo anafunsa kuti, “Chifukwa chiyani ukupita kwa iyeyo lero? Lero si tsiku la Chikondwerero cha Mwezi Watsopano kapena tsiku la Sabata.” Mayiyo anayankha kuti, “Zonse zili bwino.” Onani mutuwo |