2 Mafumu 4:22 - Buku Lopatulika22 Naitana mwamuna wake, nati, Nditumizire mmodzi wa anyamata ndi bulu mmodzi, kuti ndithamangire kwa munthu uja wa Mulungu, ndi kubweranso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Naitana mwamuna wake, nati, Nditumizire mmodzi wa anyamata ndi bulu mmodzi, kuti ndithamangire kwa munthu uja wa Mulungu, ndi kubweranso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Tsono adaitanitsa mwamuna wake, namuuza kuti, “Tumizireni wantchito mmodzi ndi bulu mmodzi, kuti ndithamangire kwa munthu wa Mulungu uja, nkubwerakonso.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Iye anayitanitsa mwamuna wake namuwuza kuti, “Tumizireni wantchito mmodzi ndi bulu mmodzi kuti ndipite mofulumira kwa munthu wa Mulungu nʼkubwererako.” Onani mutuwo |