Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 4:21 - Buku Lopatulika

21 Ndipo anakwera, namgoneka pa kama wa munthu wa Mulungu, natuluka, namtsekera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndipo anakwera, namgoneka pa kama wa munthu wa Mulungu, natuluka, namtsekera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 Pomwepo mkazi uja adanyamula mwana wake nakwera ku chipinda cham'mwamba chija, nakamgoneka pa bedi la Elisa, mtumiki wa Mulungu uja, nkumtsekera momwemo, iye nkutuluka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Mayiyo ananyamula mwanayo nakamugoneka pa bedi la munthu wa Mulungu uja. Kenaka anatseka chitseko iye nʼkuchokapo.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 4:21
6 Mawu Ofanana  

Ndipo ananena naye, Ndipatse mwana wako. Namtenga m'mfukato mwake napita naye ku chipinda chosanja chogonamo iyeyo, namgoneka pa kama wa iye mwini.


Timmangire kachipinda kosanja, timuikirenso komweko kama, ndi gome, ndi mpando, ndi choikaponyali; ndipo kudzatero kuti akatidzera alowe m'mwemo.


Namnyamula, napita naye kwa amake. Ndipo anakhala pa maondo ake kufikira usana, namwalira.


Naitana mwamuna wake, nati, Nditumizire mmodzi wa anyamata ndi bulu mmodzi, kuti ndithamangire kwa munthu uja wa Mulungu, ndi kubweranso.


Ndipo pamene Elisa analowa m'nyumba, taonani, mwanayo ngwakufa, adamgoneka pakama pake.


Pamenepo anadza, namfotokozera munthu wa Mulungu. Nati iye, Kagulitse mafuta, ukabwezere mangawa ako, ndi zotsalapo zikusunge iwe ndi ana ako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa