2 Mafumu 4:20 - Buku Lopatulika20 Namnyamula, napita naye kwa amake. Ndipo anakhala pa maondo ake kufikira usana, namwalira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Namnyamula, napita naye kwa amake. Ndipo anakhala pa maondo ake kufikira usana, namwalira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Adamunyamula, nakampereka kwa mai wake. Mwanayo adakhala pamiyendo pa mai wake mpaka masana, basi nkumwalira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Wantchito uja atamunyamula ndi kumupereka kwa amayi ake. Mwanayo anakhala pa miyendo ya amayi akeyo mpaka masana, ndipo pambuyo pake anamwalira. Onani mutuwo |