Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 4:19 - Buku Lopatulika

19 Nati kwa atate wake, Mutu wanga, mutu wanga! Pamenepo anati kwa mnyamata, Umnyamule umuke naye kwa amake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Nati kwa atate wake, Mutu wanga, mutu wanga! Pamenepo anati kwa mnyamata, Umnyamule umuke naye kwa amake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Mwadzidzidzi mwanayo adalira mofuula kwa bambo wake kuti, “Mayo! Mutu wanga ine! Mutu wanga ine!” Bambo wake uja adauza wantchito wake kuti, “Kampereke kwa mai wake.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Mwanayo anafuwula kwa abambo ake kuti, “Mayo! Mutu wanga ine! Mayo! Mutu wanga ine!” Abambo akewo anawuza wantchito wake kuti, “Munyamule ndi kukamupereka kwa amayi ake.”

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 4:19
4 Mawu Ofanana  

Ndipo atakula mwanayo, linadza tsiku lakuti anatuluka kunka kwa atate wake, ali kwa omweta tirigu.


Namnyamula, napita naye kwa amake. Ndipo anakhala pa maondo ake kufikira usana, namwalira.


Matumbo anga, matumbo anga! Ndipoteka pamtima panga penipeni; mtima wanga sukhala pansi m'kati mwanga; sindithai kutonthola; pakuti wamva, moyo wanga, mau a lipenga, mbiri ya nkhondo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa