2 Mafumu 4:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo atakula mwanayo, linadza tsiku lakuti anatuluka kunka kwa atate wake, ali kwa omweta tirigu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo atakula mwanayo, linadza tsiku lakuti anatuluka kunka kwa atate wake, ali kwa omweta tirigu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mwana uja atakula, tsiku lina adapita kwa bambo wake amene ankayang'anira anthu odula tirigu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Mwana uja anakula, ndipo tsiku lina anapita kwa abambo ake amene anali ndi anthu odula tirigu. Onani mutuwo |