2 Mafumu 4:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo mkaziyo anaima, naona mwana wamwamuna nyengo yomweyo chaka chimene chija Elisa adanena naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo mkaziyo anaima, naona mwana wamwamuna nyengo yomweyo chaka chimene chija Elisa adanena naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Koma mai uja adaimadi ndipo chaka chotsatira, nthaŵi ngati yomweyo, adabala mwana wamwamuna, monga momwe Elisa adaamuuzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Koma mayi uja anakhala woyembekezera, ndipo chaka chotsatiracho, nthawi ngati yomweyo anabereka mwana wamwamuna monga momwe Elisa anamuwuzira. Onani mutuwo |