Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 4:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo linadza tsiku lakuti anafikako, nalowa m'chipinda chosanja, nagona komweko.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo linadza tsiku lakuti anafikako, nalowa m'chipinda chosanja, nagona komweko.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsiku lina Elisa uja adafika ku Sunemu, nakaloŵa m'kachipinda kam'mwamba kaja kuti akapumule m'menemo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Tsiku lina pamene Elisa anafika ku Sunemu, iye anakalowa mʼchipinda chake chija nagona mʼmenemo.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 4:11
3 Mawu Ofanana  

Timmangire kachipinda kosanja, timuikirenso komweko kama, ndi gome, ndi mpando, ndi choikaponyali; ndipo kudzatero kuti akatidzera alowe m'mwemo.


Nati kwa Gehazi mnyamata wake, Itana Msunamu uja. Namuitana, naima mkaziyo pamaso pake.


Ndipo linafika tsiku lakuti Elisa anapitirira kunka ku Sunemu, kumeneko kunali mkazi womveka; ameneyo anamuumiriza adye mkate. Potero pomapitirako iyeyo, ankawapatukirako kukadya mkate.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa