2 Mafumu 4:10 - Buku Lopatulika10 Timmangire kachipinda kosanja, timuikirenso komweko kama, ndi gome, ndi mpando, ndi choikaponyali; ndipo kudzatero kuti akatidzera alowe m'mwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Timmangire kachipinda kosanja, timuikirenso komweko kama, ndi gome, ndi mpando, ndi choikapo nyali; ndipo kudzatero kuti akatidzera alowe m'mwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tiyeni timmangire kachipinda kakang'ono kam'mwamba, ndipo timuikiremo bedi, tebulo, mpando ndi nyale, kuti nthaŵi zonse akatichezera, azitha kumakakhala m'menemo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Tiyeni timumangire kachipinda kakangʼono pa denga la nyumbayi ndi kumuyikiramo bedi ndi tebulo, mpando ndi nyale. Akabwera kuno azikhala mʼmenemo.” Onani mutuwo |