Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




2 Mafumu 3:5 - Buku Lopatulika

5 Koma kunachitika, atafa Ahabu mfumu ya Mowabu anapandukana ndi mfumu ya Israele.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Koma kunachitika, atafa Ahabu mfumu ya Mowabu anapandukana ndi mfumu ya Israele.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Koma Ahabu atamwalira, mfumu ya Amowabuyo idagalukira mfumu ya ku Israele.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Koma atamwalira Ahabu, mfumu ya ku Mowabu inawukira mfumu ya ku Israeli.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 3:5
5 Mawu Ofanana  

Ndipo atamwalira Ahabu, Mowabu anapandukana ndi Israele.


Pamenepo Elisa anamwalira, ndipo anamuika. Ndipo magulu a Amowabu analowa m'dziko poyambira chaka.


Ndipo mfumu Yehoramu anatuluka mu Samariya nthawi yomweyo, namemeza Aisraele onse.


Masiku ake Aedomu anapanduka ku ulamuliro wa Yuda, nadziikira mfumu okha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa