2 Mafumu 3:23 - Buku Lopatulika23 nati, Uja ndi mwazi, atha kuonongana mafumu aja, anakanthana wina ndi mnzake; ndipo tsopano, tiyeni Amowabu inu, tikafunkhe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 nati, Uja ndi mwazi, atha kuonongana mafumu aja, anakanthana wina ndi mnzake; ndipo tsopano, tiyeni Amowabu inu, tikafunkhe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono adati, “Taonani magazi! Mafumu aja amenyana okhaokha, ndipo ankhondo ao aphana. Tiyeni tikafunkhe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Ndipo iwo anati, “Taonani magazi! Mafumu aja amenyana okhaokha ndipo aphana. Amowabu, tsopano ndi nthawi yofunkha!” Onani mutuwo |