2 Mafumu 3:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo pamene anauka mamawa dzuwa linawala pamadzipo, naona Amowabu madzi ali pandunji pao ali psu ngati mwazi; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo pamene anauka mamawa dzuwa linawala pamadzipo, naona Amowabu madzi ali pandunji pao ali psu ngati mwazi; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Amowabuwo atadzuka m'mamaŵa pamene dzuŵa linkaŵala pa madzi, adaona madzi ali psuu ngati magazi kutsogolo kwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Amowabu atadzuka mmamawa, dzuwa likuwala pa madziwo, anaona madziwo akuoneka wofiira ngati magazi patsogolo pawo. Onani mutuwo |