2 Mafumu 3:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo kunachitika m'mawa, pomapereka nsembe yaufa, taonani, anafika madzi odzera ku Edomu; ndipo dziko linadzala ndi madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo kunachitika m'mawa, pomapereka nsembe yaufa, taonani, anafika madzi odzera ku Edomu; ndipo dziko linadzala ndi madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 M'maŵa mwake, nthaŵi yopereka nsembe ili pafupi, adangoona madzi akutuluka kuchokera ku Edomu, mpaka malowo adadzaza madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mmawa mwake, nthawi yopereka nsembe ili pafupi, anangoona madzi akutuluka kuchokera ku Edomu, ndipo malo onse anadzaza ndi madzi. Onani mutuwo |