2 Mafumu 3:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo mudzakantha mizinda yonse ya malinga, ndi mizinda yonse yosankhika, ndi kulikha mitengo yonse yabwino, ndi kufotsera zitsime zonse zamadzi, ndi kuipitsa pa nthaka ponse pabwino ndi miyala. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo mudzakantha midzi yonse ya malinga, ndi midzi yonse yosankhika, ndi kulikha mitengo yonse yabwino, ndi kufotsera zitsime zonse zamadzi, ndi kuipitsa pa nthaka ponse pabwino ndi miyala. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Mudzagonjetsa mizinda yao yonse yamalinga ndi yabwinoyabwino ija. Mudzagwetsa mitengo yabwino yonse ndi kutseka akasupe onse a madzi, ndipo mudzaononga minda yao yonse yachonde, pakuponyamo miyala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mudzagonjetsa mizinda yawo yonse yotetezedwa ndiponso mizinda yawo ikuluikulu. Mudzagwetsa mtengo wabwino uliwonse, mudzatseka akasupe onse amadzi, ndiponso mudzawononga minda yawo yonse yachonde poponyamo miyala.” Onani mutuwo |