Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 3:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo anati, Atero Yehova, Kumbani m'chigwa muno mukhale maenje okhaokha.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo anati, Atero Yehova, Kumbani m'chigwa muno mukhale maenje okhaokha.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Tsono adati, “Chauta akuti, ‘Mukumbe migwere mu mtsinje wopanda madziwu, ndipo Ine ndidzadzazamo madzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 ndipo anati, “Yehova akuti, ‘Kumbani ngalande mʼchigwa chonse.’

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 3:16
4 Mawu Ofanana  

Koma tsopano, nditengereni wanthetemya. Ndipo kunali, wanthetemyayo ali chiimbire, dzanja la Yehova linamgwera.


Pakuti atero Yehova, Simudzaona mphepo, kapena kuona mvula, koma chigwacho chidzadzala ndi madzi; ndipo mudzamwa inu, ndi ng'ombe zanu, ndi zoweta zanu.


Pamenepo anati, Kabwereke zotengera kwina kwa anansi ako onse, zotengera zopanda kanthu, zisakhale pang'ono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa