2 Mafumu 3:12 - Buku Lopatulika12 Nati Yehosafati, Mau a Yehova ali ndi iyeyo. Pamenepo mfumu ya Israele, ndi Yehosafati, ndi mfumu ya Edomu, anatsikira kuli iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Nati Yehosafati, Mau a Yehova ali ndi iyeyo. Pamenepo mfumu ya Israele, ndi Yehosafati, ndi mfumu ya Edomu, anatsikira kuli iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pomwepo Yehosafati adati, “Elisayo ndiye mneneri weniweni wa Chauta.” Choncho mafumu atatu aja adapita kwa mneneri Elisa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Yehosafati anati, “Yehova amayankhula kudzera mwa iye.” Choncho mfumu ya ku Israeli pamodzi ndi Yehosafati ndiponso mfumu ya ku Edomu anapita kwa Elisa. Onani mutuwo |