2 Mafumu 25:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo mzindawo unazingidwa ndi timalinga mpaka chaka chakhumi ndi chimodzi cha mfumu Zedekiya. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo mudziwo unazingidwa ndi timalinga mpaka chaka chakhumi ndi chimodzi cha mfumu Zedekiya. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Motero mzindawo udaazingidwa ndi zithandozo mpaka chaka cha 11 cha ufumu wa Zedekiya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Mzindawo anawuzinga mpaka chaka cha khumi ndi chimodzi cha Mfumu Zedekiya. Onani mutuwo |