2 Mafumu 24:9 - Buku Lopatulika9 Nachita iye choipa pamaso pa Yehova, monga umo monse adachita atate wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Nachita iye choipa pamaso pa Yehova, monga umo monse adachita atate wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yehoyakini adachita zoipa pamaso pa Chauta potsata zonse zimene ankachita bambo wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iye anachita zoyipa pamaso pa Yehova monga anachitira abambo ake. Onani mutuwo |