2 Mafumu 24:11 - Buku Lopatulika11 Nafika Nebukadinezara mfumu ya Babiloni kumzinda, ataumangira misasa anyamata ake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nafika Nebukadinezara mfumu ya Babiloni kumudzi, ataumangira misasa anyamata ake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndipo Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni adafika ku mzindawo pa nthaŵi imene ankhondo ake ankauzinga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 ndipo Nebukadinezara anafika ku mzindawo pamene ankhondo ake anawuzinga. Onani mutuwo |