2 Mafumu 23:7 - Buku Lopatulika7 Nagamula nyumba za anyamata adama okhala kunyumba ya Yehova, kumene akazi anaomba nsalu zolenjeka za chifanizocho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nagamula nyumba za anyamata adama okhala kunyumba ya Yehova, kumene akazi anaomba nsalu zolenjeka za chifanizocho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adagwetsa tinyumba ta amuna ochitana zadama ku Nyumba ya Mulungu, ku malo amene akazi ankalukira mikanjo yovala anthu opembedza Asera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iye anagwetsanso tinyumba ta ochita zachiwerewere, timene tinali mʼNyumba ya Yehova, kumene akazi ankalukirako mikanjo yovala popembedza Asera. Onani mutuwo |