Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




2 Mafumu 23:18 - Buku Lopatulika

18 Nati iye, Mlekeni, munthu asakhudze mafupa ake. Naleka iwo mafupa ake akhale pamodzi ndi mafupa a mneneri uja anatuluka mu Samariya.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Nati iye, Mlekeni, munthu asakhudze mafupa ake. Naleka iwo mafupa ake akhale pamodzi ndi mafupa a mneneri uja anatuluka m'Samariya.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Yosiya adati, “Mlekeni. Munthu asachotse mafupa akewo ai.” Motero mafupawo adangoŵaleka pamodzi ndi mafupa a mneneri wa ku Samariya uja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Mfumuyo inati, “Alekeni manda amenewo, munthu asachotse mafupa ake.” Choncho anawasiya mafupa akewo pamodzi ndi mafupa a mneneri wa ku Samariya uja.

Onani mutuwo Koperani




2 Mafumu 23:18
3 Mawu Ofanana  

Ndipo mneneri ananyamula mtembo wa munthu wa Mulunguyo, nausenza pabulu, nabwera nao, nalowa m'mzinda mneneri wokalamba kumlira ndi kumuika.


Ndipo kunachitika, atamuika iye, ananena ndi ana ake, nati, Nkadzamwalira ine mudzandiike ine m'manda momwemo mwaikidwa munthu wa Mulunguyo, ikani mafupa anga pafupi ndi mafupa ake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa