2 Mafumu 23:1 - Buku Lopatulika1 Pamenepo mfumu inatumiza anthu, namsonkhanitsira akulu onse a Yuda ndi a mu Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pamenepo mfumu inatumiza anthu, namsonkhanitsira akulu onse a Yuda ndi a m'Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamenepo mfumu Yosiya adatumiza mau kukaitana akuluakulu onse a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu kuti adzasonkhane. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Pamenepo mfumu inayitanitsa akuluakulu onse a ku Yuda ndi Yerusalemu. Onani mutuwo |