2 Mafumu 22:5 - Buku Lopatulika5 ndizo zimene olindira pakhomo anasonkhetsa anthu; azipereke m'dzanja la antchito akuyang'anira nyumba ya Yehova; iwo azipereke kwa ogwira ntchito ya m'nyumba ya Yehova, akonze mogamuka nyumbayi, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 iwo azipereke kwa ogwira ntchito ya m'nyumba ya Yehova, akonze mogamuka nyumbayi, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Ndalama zimenezo azipereke kwa akapitao okonzetsa Nyumba ya Chauta aja. Iwowo azipereke kwa antchito aja okonza Nyumba ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndalamazo azipereke kwa anthu amene asankhidwa kuti ayangʼanire ntchito ya Nyumba ya Yehova. Ndipo anthu amenewa azilipira antchito amene akukonzanso Nyumba ya Yehova, Onani mutuwo |