2 Mafumu 22:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo mfumu inalamulira Hilikiya wansembe, ndi Ahikamu mwana wa Safani, ndi Akibori mwana wa Mikaya, ndi Safani mlembi, ndi Asaya mnyamata wa mfumu, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo mfumu inalamulira Hilikiya wansembe, ndi Ahikamu mwana wa Safani, ndi Akibori mwana wa Mikaya, ndi Safani mlembi, ndi Asaya mnyamata wa mfumu, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Pomwepo idalamula wansembe Hilikiya, Ahikamu mwana wa Safani, Akibori mwana wa Mikaya, Safani mlembi uja ndi Asaya mtumiki wa mfumu, kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Iyo inalamula wansembe Hilikiya, Ahikamu mwana wa Safani, Akibo mwana wa Mikaya, Safani mlembi uja ndi Asaiya mtumiki wa mfumu, kuti, Onani mutuwo |