2 Mafumu 22:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo kunali, atamva mfumu mau a m'buku la chilamulo, inang'amba zovala zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo kunali, atamva mfumu mau a m'buku la chilamulo, inang'amba zovala zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mfumu itamva mau a m'buku la Malamulo, idang'amba zovala zake mwachisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mfumu itamva mawu a mʼBuku la Malamulo, inangʼamba zovala zake. Onani mutuwo |