2 Mafumu 22:10 - Buku Lopatulika10 Ndipo Safani mlembiyo anafotokozera mfumu, ndi kuti, Hilikiya wansembe wandipatsa buku. Nawerengamo Safani pamaso pa mfumu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Ndipo Safani mlembiyo anafotokozera mfumu, ndi kuti, Hilikiya wansembe wandipatsa buku. Nawerengamo Safani pamaso pa mfumu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono Safani adauza mfumu kuti, “Wansembe Hilikiya wandipatsira buku.” Ndipo Safani adaliŵerenga bukulo pamaso pa mfumu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Kenaka Safani mlembiyo, anafotokozera mfumu kuti, “Wansembe Hilikiya wandipatsa buku.” Ndipo Safani analiwerenga pamaso pa mfumu. Onani mutuwo |